Levitiko 7:5 - Buku Lopatulika5 ndipo wansembe atenthe izi paguwa la nsembe, nsembe yamoto ya kwa Yehova; ndiyo nsembe yopalamula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndipo wansembe atenthe izi pa guwa la nsembe, nsembe yamoto ya kwa Yehova; ndiyo nsembe yopalamula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Wansembe azitenthere pa guwa zonsezo, kuti zikhale nsembe yotentha pa moto, yopereka kwa Chauta. Imeneyo ndiyo nsembe yopepesera kupalamula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Wansembe azitenthe pa guwa kuti zikhale nsembe yotentha pa moto, yoperekedwa kwa Yehova. Imeneyi ndi nsembe yopepesera tchimo lopalamula. Onani mutuwo |