Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 7:4 - Buku Lopatulika

4 ndi impso ziwiri, ndi mafuta a pamenepo, okhala m'chuuno, ndi chokuta cha mphafa chofikira kuimpso;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 ndi impso ziwiri, ndi mafuta a pamenepo, okhala m'chuuno, ndi chokuta cha mphafa chofikira kuimpso;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Aperekenso imso ziŵiri pamodzi ndi mafuta ake omwe cham'chiwunomu, ndiponso mphumphu ya mafuta akuchiŵindi ochotsa ndi imso zija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Aperekenso impsyo ziwiri, mafuta ake pamodzi ndi mafuta onse amene ali chamʼchiwuno, ndiponso mafuta onse amene aphimba chiwindi.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 7:4
4 Mawu Ofanana  

Nutenge mafuta onse akukuta matumbo, ndi chokuta cha mphafa ndi impso ziwiri, ndi mafuta ali pa izo, ndi kuzitentha paguwa la nsembe.


ndi impso ziwiri, ndi mafuta ali pomwepo, okhala m'chuuno, ndi chokuta cha mphafa chofikira kuimpso.


ndi impso ziwiri, ndi mafuta ali pomwepo okhala m'chuuno, ndi chokuta cha mphafa chofikira kuimpso.


ndipo wansembe atenthe izi paguwa la nsembe, nsembe yamoto ya kwa Yehova; ndiyo nsembe yopalamula.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa