Levitiko 7:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo achotseko, nabwere nao mafuta ake onse; mchira wamafuta, ndi mafuta akukuta matumbo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo achotseko, nabwere nao mafuta ake onse; mchira wamafuta, ndi mafuta akukuta matumbo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono apereke mafuta ake onse, mchira wamafuta ndi mafuta okuta matumbo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsono apereke mafuta ake onse: mchira wamafuta ndi mafuta amene amakuta matumbo. Onani mutuwo |