Levitiko 7:2 - Buku Lopatulika2 Pamalo pophera nsembe yopsereza ndipo aziphera nsembe yopalamula; nawaze mwazi wake paguwa la nsembe pozungulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pamalo pophera nsembe yopsereza ndipo aziphera nsembe yopalamula; nawaze mwazi wake pa guwa la nsembe pozungulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 pamalo pomwe amaphera nsembe yopsereza, azipheraponso nsembe yopepesera kupalamula, ndipo awaze magazi ake pa guwa mozungulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Nsembe yopepesera machimo iziphedwa pamalo pomwe amaphera nsembe yopsereza ndipo awaze magazi ake mbali zonse za guwa. Onani mutuwo |