Levitiko 7:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo akadyako nyama ya nsembe zoyamika zake tsiku lachitatu, sikuvomerezeka kumene; sadzamwerengera wobwera nayo; ndiyo chinthu chonyansa, ndipo munthu wakudyako adzasenza mphulupulu zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo akadyako nyama ya nsembe zoyamika zake tsiku lachitatu, sikuvomerezeka kumene; sadzamwerengera wobwera nayo; ndiyo chinthu chonyansa, ndipo munthu wakudyako adzasenza mphulupulu zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ngati munthu adya nyama ya nsembe yachiyanjano pa tsiku lachitatu, amene waiperekayo Mulungu sadzamulandira, ndipo nsembeyo sidzampindulira kanthu. Idzakhala chinthu chonyansa ndipo amene adzadye imeneyo adzakhala wopalamula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ngati munthu adya nyama yachiyanjano pa tsiku lachitatu, nsembeyo sidzalandiridwa. Amene wayipereka nsembeyo Mulungu sadzamulandira ndipo nsembeyo idzakhala yonyansa pamaso pa Mulungu, yosamupindulira kanthu woperekayo. Onani mutuwo |