Levitiko 7:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo nyama yokhudza kanthu kalikonse kodetsa isadyeke; aitenthe ndi moto. Koma za nyama ina, aliyense ayera aidyeko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo nyama yokhudza kanthu kalikonse kodetsa isadyeke; aitenthe ndi moto. Koma za nyama ina, aliyense ayera aidyeko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 “Nyama imene ikhudza chinthu chilichonse chonyansa pa zachipembedzo, munthu asaidye, koma itenthedwe pa moto. Onse amene ali osaipitsidwa pa zachipembedzo angathe kudya nyama ya nsembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 “ ‘Nyama imene yakhudza chilichonse chodetsedwa, munthu asayidye, koma itenthedwe pa moto. Aliyense amene ali woyeretsedwa angathe kudya nyama inayo. Onani mutuwo |