Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 7:17 - Buku Lopatulika

17 koma chotsalira pa nyama ya nsembeyo tsiku lachitatu, achitenthe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 koma chotsalira pa nyama ya nsembeyo tsiku lachitatu, achitenthe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Koma nyama yotsalako kufikira tsiku lachitatu, aitenthe pa moto.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ngati nyama ina ya nsembe yatsalabe mpaka tsiku lachitatu, imeneyo itenthedwe pa moto.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 7:17
11 Mawu Ofanana  

Tsiku lachitatu Abrahamu anatukula maso ake naona malowo patali.


Ndipo musasiyako kufikira m'mawa; koma yotsalira kufikira m'mamawayo muipsereze ndi moto.


Nakonzekeretu tsiku lachitatu; pakuti tsiku lachitatu Yehova adzatsika paphiri la Sinai pamaso pa anthu onse.


Koma nyama ya ng'ombeyo, ndi chikopa chake, ndi chipwidza chake, uzitentha izi ndi moto kunja kwa chigono; ndiyo nsembe yauchimo.


Ndipo ikatsalako nyama yodzaza manja, kapena mkate kufikira m'mawa, pamenepo utenthe zotsalazo ndi moto; asazidye popeza nchopatulika ichi.


Atapita masiku awiri adzatitsitsimutsa, tsiku lachitatu adzatiutsa; ndipo tidzakhala ndi moyo pamaso pake.


Ndipo Mose anafunafuna mbuzi ya nsembe yauchimo, ndipo taonani, adaitentha. Ndipo anapsa mtima pa Eleazara ndi Itamara, ana otsalawo a Aroni, nati,


Tsiku lomwelo mwaipha, ndi m'mawa mwake muidye; ngati katsalirako kanthu tsiku lachitatu, muzikatentha ndi moto.


Akakadya konse tsiku lachitatu kali chonyansa, kosavomerezeka:


ndi kuti anaikidwa; ndi kuti anaukitsidwa tsiku lachitatu, monga mwa malembo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa