Levitiko 7:17 - Buku Lopatulika17 koma chotsalira pa nyama ya nsembeyo tsiku lachitatu, achitenthe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 koma chotsalira pa nyama ya nsembeyo tsiku lachitatu, achitenthe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma nyama yotsalako kufikira tsiku lachitatu, aitenthe pa moto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ngati nyama ina ya nsembe yatsalabe mpaka tsiku lachitatu, imeneyo itenthedwe pa moto. Onani mutuwo |