Levitiko 7:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo chilamulo cha nsembe zoyamika, zimene azibwera nazo kwa Yehova ndi ichi: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo chilamulo cha nsembe zoyamika, zimene azibwera nazo kwa Yehova ndi ichi: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Lamulo la nsembe yachiyanjano imene aliyense angathe kupereka kwa Chauta ndi ili: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “ ‘Malamulo a nsembe ya chiyanjano imene munthu angathe kupereka kwa Yehova ndi awa: Onani mutuwo |