Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 7:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo nsembe zonse zaufa zosakaniza ndi mafuta, kapena zouma zikhale za ana onse a Aroni, alandireko onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo nsembe zonse zaufa zosanganiza ndi mafuta, kapena zouma zikhale za ana onse a Aroni, alandireko onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Ndipo chopereka chilichonse cha chakudya chosakaniza ndi mafuta kapena chouma, chikhale cha ana onse a Aroni. Anawo aigaŵane molingana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ndipo chopereka china chilichonse cha chakudya chosakaniza ndi mafuta kapena chowuma, chikhale cha ana onse a Aaroni ndipo anawo achigawane mofanana.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 7:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anayesa ndi omeri, iye amene adaola wambiri sunamtsalire, ndi iye amene adaola pang'ono sunamsowe; yense anaola monga mwa njala yake.


Ndipo chilamulo cha nsembe zoyamika, zimene azibwera nazo kwa Yehova ndi ichi:


Ndipo nsembe zaufa zonse zophika mumchembo, ndi zonse zokonzeka mumphika, ndi pachiwaya, zikhale za wansembe amene wabwera nazo.


koma mwa kulingana kuchuluka kwanu kukwanire kusowa kwao nthawi ya makono ano, kutinso kuchuluka kwao kukwanire kusowa kwanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa