Levitiko 4:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo wansembe wodzozedwayo adze nao mwazi wina wa ng'ombeyo ku chihema chokomanako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo wansembe wodzozedwayo adze nao mwazi wina wa ng'ombeyo ku chihema chokomanako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Wansembe wodzozedwa atengeko magazi a ng'ombe yamphongoyo ndi kubwera nawo ku chihema chamsonkhano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tsono wansembe wodzozedwa atengeko magazi a ngʼombeyo ndi kulowa nawo mu tenti ya msonkhano. Onani mutuwo |