Levitiko 4:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo akulu a khamulo aike manja ao pamutu pa ng'ombeyo, pamaso pa Yehova; naiphe ng'ombeyo pamaso pa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo akulu a khamulo aike manja ao pamutu pa ng'ombeyo, pamaso pa Yehova; naiphe ng'ombeyo pamaso pa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Apo atsogoleri a mpingo asanjike manja ao pamutu pa ng'ombe yamphongoyo pamaso pa Chauta, ndipo aiphe pamaso pa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Akuluakulu a anthuwo asanjike manja awo pa mutu pa ngʼombe pamaso pa Yehova, ndipo ayiphe pomwepo pamaso pa Yehova. Onani mutuwo |