Levitiko 3:3 - Buku Lopatulika3 Pamenepo abwere nayo nsembe yamoto ya kwa Yehova, yotengako ku nsembe yoyamika; achotse mafuta akukuta matumbo, ndi mafuta onse akukhala pamatumbo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamenepo abwere nayo nsembe yamoto ya kwa Yehova, yotengako ku nsembe yoyamika; achotse mafuta akukuta matumbo, ndi mafuta onse akukhala pamatumbo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndipo pa nsembe yachiyanjanoyo, yopereka kwa Chauta ndi yoyenera kuitentha pa moto, atapepo mafuta okuta matumbo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pa nsembe yachiyanjanopo, ayenera kupatula zamʼkati mwa nyamayo ndi mafuta onse amene amakuta zamʼkati kupereka nsembe ya chakudya kwa Yehova. Onani mutuwo |