Levitiko 3:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo aike dzanja lake pamutu wa chopereka chake, ndi kuipha pa chipata cha chihema chokomanako; ndipo ana a Aroni, ansembewo, awaze mwazi wake paguwa la nsembe pozungulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo aike dzanja lake pa mutu wa chopereka chake, ndi kuipha pa chipata cha chihema chokomanako; ndipo ana a Aroni, ansembewo, awaze mwazi wake pa guwa la nsembe pozungulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Munthuyo asanjike dzanja lake pamutu pa ng'ombeyo, ndipo aiphere pa khomo la chihema chamsonkhano. Pomwepo ansembe, ana a Aroni, aliwaze magazi guwa molizungulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Munthuyo asanjike dzanja lake pamutu pa ngʼombeyo, ndipo ayiphere pa khomo la tenti ya msonkhano. Ndipo ansembe, ana a Aaroni, awaze magazi mbali zonse za guwalo. Onani mutuwo |