Levitiko 3:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo chopereka chake chikakhala nsembe yoyamika; akabwera nayo ng'ombe, kapena yaimuna kapena yaikazi, azibwera nayo yopanda chilema pamaso pa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo chopereka chake chikakhala nsembe yoyamika; akabwera nayo ng'ombe, kapena yaimuna kapena yaikazi, azibwera nayo yopanda chilema pamaso pa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Ngati munthu apereka nsembe yachiyanjano kwa Chauta, nsembe yake ikakhala ya ng'ombe yamphongo kapena yaikazi, ikhale yopanda chilema. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “ ‘Ngati munthu apereka nsembe ya chiyanjano kwa Yehova, ndipo choperekacho nʼkukhala ngʼombe yayimuna kapena yayikazi, ikhale yopanda chilema. Onani mutuwo |