Levitiko 3:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo wansembe atenthe izi paguwa la nsembe; ndizo chakudya cha nsembe yamoto ichite fungo lokoma; mafuta onse nga Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo wansembe atenthe izi pa guwa la nsembe; ndizo chakudya cha nsembe yamoto ichite fungo lokoma; mafuta onse nga Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Wansembe atenthe zonsezo pa guwa, kuti zikhale chakudya chotentha pa moto, cha fungo lokoma. Mafuta onse nga Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Wansembe awotche zonsezi pa guwa. Ichi ndi chakudya cha Yehova, chowotcha pa moto ndiponso cha fungo lokomera Yehova. Mafuta onse ndi a Yehova. Onani mutuwo |