Levitiko 3:17 - Buku Lopatulika17 Likhale lemba losatha m'mibadwo yanu m'nyumba zanu zonse, musamadya kapena mafuta kapena mwazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Likhale lemba losatha m'mibadwo yanu m'nyumba zanu zonse, musamadya kapena mafuta kapena mwazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Limeneli likhale lamulo lamuyaya pa mibadwo yanu yonse, kuti musadzadye mafuta kapena magazi kulikonse kumene mudzakhale.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 “ ‘Limeneli likhale lamulo lamuyaya pa mibado yanu yonse kuti musadzadye mafuta kapena magazi kulikonse kumene mudzakhale.’ ” Onani mutuwo |