Levitiko 26:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ndidzatembenukira kwa inu, ndi kukubalitsani, ndi kukuchulukitsani; ndipo ndidzakhazika chipangano changa ndinapangana nanucho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ndidzatembenukira kwa inu, ndi kukubalitsani, ndi kukuchulukitsani; ndipo ndidzakhazika chipangano changa ndinapangana nanucho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndidzakukumbukirani, ndipo ndidzakubalitsani ana ambiri ndi kukuchulukitsani. Ndidzalimbitsa chipangano changa ndi inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “ ‘Ndidzakukumbukirani ndi kukupatsani ana ambiri ndi kukuchulukitsani. Ndidzasunga pangano langa ndi inu. Onani mutuwo |