Levitiko 26:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo mudzadya za sundwe wakale ndi kutulutsa zakale chifukwa cha zatsopano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo mudzadya za sundwe wakale ndi kutulutsa zakale chifukwa cha zatsopano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Muzidzadyabe sundwe wakalekale, koma mudzachotsa sundweyo m'khokwe, kuti zatsopano zipeze malo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mudzakhala mukudyabe chakudya chogonera ndipo mudzachotse chakudyacho mʼnkhokwe kuti mupezemo malo woyika chakudya china chatsopano. Onani mutuwo |