Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 26:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo mudzadya za sundwe wakale ndi kutulutsa zakale chifukwa cha zatsopano.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo mudzadya za sundwe wakale ndi kutulutsa zakale chifukwa cha zatsopano.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Muzidzadyabe sundwe wakalekale, koma mudzachotsa sundweyo m'khokwe, kuti zatsopano zipeze malo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Mudzakhala mukudyabe chakudya chogonera ndipo mudzachotse chakudyacho mʼnkhokwe kuti mupezemo malo woyika chakudya china chatsopano.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 26:10
5 Mawu Ofanana  

Ndi ichi ndi chizindikiro chako: chaka chino mudzadya za mphulumukwa, ndi chaka cha mawa za mankhokwe, ndi chaka chamkucha muzibzala ndi kukolola, muzioka minda yampesa ndi kudya zipatso zake.


Ndipo madwale adzakhala ndi tirigu, ndi vinyo, ndi mafuta; zidzasefuka m'zosungiramo zao.


Ndipo mubzale chaka chachisanu ndi chitatu, ndi kudya zipatso zasundwe; kufikira chaka chachisanu ndi chinai, mpaka zitacha zipatso zake mudzadya zasundwe.


Ndipo anaganizaganiza mwa yekha nanena, Ndidzatani ine, popeza ndilibe mosungiramo zipatso zanga?


Ndipo m'mawa mwake atatha Paska, anadya tirigu wakhwimbi wa m'dziko, mikate yopanda chotupitsa ndi tirigu wokazinga tsiku lomwe lija.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa