Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 26:2 - Buku Lopatulika

2 Musunge masabata anga, ndi kuchitira ulemu malo anga opatulika; Ine ndine Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Musunge masabata anga, ndi kuchitira ulemu malo anga opatulika; Ine ndine Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Muzisunga masiku anga a Sabata ndi kulemekeza malo anga oyera. Ine ndine Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “ ‘Muzisunga Masabata anga ndipo muzilemekeza malo anga wopatulika. Ine ndine Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 26:2
3 Mawu Ofanana  

Udzikumbukira tsiku la Sabata, likhale lopatulika.


Koma iwe, lankhula ndi ana a Israele, ndi kuti, Muzisunga masabata anga ndithu; pakuti ndiwo chizindikiro pakati pa Ine ndi inu mwa mibadwo yanu; kuti mudziwe kuti Ine ndine Yehova wakukupatulani.


Muzisunga masabata anga, ndi kuchitira ulemu malo anga opatulika; Ine ndine Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa