Levitiko 2:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo wansembeyo atengeko chikumbutso pa nsembe yaufa, nachitenthe paguwa la nsembe; ndicho nsembe yamoto ya fungo lokoma la kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo wansembeyo atengeko chikumbutso pa nsembe yaufa, nachitenthe pa guwa la nsembe; ndicho nsembe yamoto ya fungo lokoma la kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Apo wansembeyo atengeko gawo lina la choperekacho kusonyeza kuti chaperekedwa kwa Chauta, tsono achitenthe paguwapo. Imeneyo ndiyo nsembe yotentha pa moto, ya fungo lokomera Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Wansembeyo atengeko gawo lina la nsembeyo kukhala ufa wachikumbutso kuti ilandiridwe ndi Yehova mʼmalo mwa nsembe yonse ndipo ayitenthe pa moto monga nsembe yopsereza ya fungo lokomera Yehova. Onani mutuwo |