Levitiko 2:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo chotsalira cha nsembe yaufa chikhale cha Aroni ndi ana ake; ndicho chopatulika kwambiri cha nsembe zamoto za Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo chotsalira cha nsembe yaufa chikhale cha Aroni ndi ana ake; ndicho chopatulika kwambiri cha nsembe zamoto za Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndipo zotsala za chopereka cha chakudyacho zikhale za Aroni ndi ana ake. Chimenecho ndicho chigawo chopatulika kopambana, chifukwa chatapidwa pa nsembe yotentha pa moto, yopereka kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Zotsala za nsembe ya chakudyayo zikhale za Aaroni ndi ana ake. Chimenechi ndi chigawo chopatulika kwambiri chifukwa chatapidwa pa chopereka chotentha pa moto cha Yehova. Onani mutuwo |