Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 2:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo chopereka chako chikakhala nsembe yaufa ya mumphika, chikhale cha ufa wosalala ndi mafuta.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo chopereka chako chikakhala nsembe yaufa ya mumphika, chikhale cha ufa wosalala ndi mafuta.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ndipo nsembe yako ikakhala ya chopereka cha chakudya chophika pa chiwaya, chikhale ya ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Ngati nsembe yako yachakudya ndi yophikidwa pa chiwaya, ikhale ya buledi wa ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 2:7
5 Mawu Ofanana  

ya mkate woonekera womwe, ndi ya ufa wosalala wa nsembe yaufa, ndi ya timitanda taphanthiphanthi topanda chotupitsa, ndi ya chiwaya, ndi yakukazinga, ndi ya miyeso iliyonse;


Uphwanye, nuthirepo mafuta; ndiyo nsembe yaufa.


Ndipo ubwere nayo nsembe yaufa yopangika ndi izi kwa Yehova; ndipo atabwera nacho kwa wansembe, iyeyo apite nacho ku guwa la nsembe.


Ndipo nsembe zaufa zonse zophika mumchembo, ndi zonse zokonzeka mumphika, ndi pachiwaya, zikhale za wansembe amene wabwera nazo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa