Levitiko 16:3 - Buku Lopatulika3 Aroni azilowa pa bwalo la malo opatulika nazozo: ng'ombe yamphongo ikhale ya nsembe yauchimo, ndi nkhosa yamphongo ikhale ya nsembe yopsereza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Aroni azilowa pa bwalo la malo opatulika nazozo: ng'ombe yamphongo ikhale ya nsembe yauchimo, ndi nkhosa yamphongo ikhale ya nsembe yopsereza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Koma Aroniyo aziloŵa m'malo opatulikawo motere: azitenga mwanawang'ombe wamphongo kuti akhale nsembe yopepesera machimo, ndi nkhosa yamphongo kuti ikhale nsembe yopsereza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Aaroni azilowa Malo Wopatulika Kwambiri motere: azitenga mwana wangʼombe wamwamuna kuti akhale nsembe yopepesera machimo ndi nkhosa yayimuna kuti ikhale nsembe yopsereza. Onani mutuwo |