Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 12:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo akhale m'mwazi wa kumyeretsa kwake masiku makumi atatu kudza atatu; asakhudze kanthu kopatulika, kapena kulowa m'malo opatulika, kufikira adakwanira masiku a kumyeretsa kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo akhale m'mwazi wa kumyeretsa kwake masiku makumi atatu kudza atatu; asakhudze kanthu kopatulika, kapena kulowa m'malo opatulika, kufikira adakwanira masiku a kumyeretsa kwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mkaziyo adikirebe masiku ena 33, kuti ayeretsedwe ku matenda ake. Asakhudze kanthu kopatulika kalikonse, ndipo asaloŵe m'malo oyera, mpaka masiku akudziyeretsa atatha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Mkaziyo adikire masiku ena 33 kuti ayeretsedwe ku matenda ake. Asakhudze kanthu kalikonse koyera kapena kulowa mʼmalo wopatulika mpaka masiku a kuyeretsedwa kwake atatha.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 12:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo tsiku lachisanu ndi chitatu adule khungu la mwanayo.


Koma akabala mwana wamkazi, akhale wodetsedwa masabata awiri, monga umo amakhala padera; ndipo adzakhala m'mwazi wa kumyeretsa kwake masiku makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi limodzi.


Pamenepo Hagai anati, Munthu wodetsedwa ndi mtembo akakhudza kanthu ka izi, kodi kali kodetsedwa kanthuka? Ndipo ansembe anayankha nati, Kadzakhala kodetsedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa