Levitiko 10:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo panatuluka moto pamaso pa Yehova, nuwatha, nafa iwo pamaso ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo panatuluka moto pamaso pa Yehova, nuwatha, nafa iwo pamaso ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono Chauta adatumiza moto nuŵapsereza, ndipo onsewo adafa pamaso pa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Choncho moto unatuluka pamaso pa Yehova ndi kuwapsereza, ndipo anafa pamaso pa Yehova. Onani mutuwo |