Levitiko 10:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo ana a Aroni, Nadabu ndi Abihu anatenga yense mbale yake ya zofukiza, naikamo moto, naikapo chofukiza, nabwera nao pamaso pa Yehova moto wachilendo, umene sanawauze. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo ana a Aroni, Nadabu ndi Abihu anatenga yense mbale yake ya zofukiza, naikamo moto, naikapo chofukiza, nabwera nao pamaso pa Yehova moto wachilendo, umene sanawauze. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ana a Aroni, Nadabu ndi Abihu, aliyense adatenga chofukizira lubani naikamo makala amoto. Pamakalapo adathirapo lubani, ndipo adapereka kwa Chauta moto umene Iye sadalamule. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ana a Aaroni, Nadabu ndi Abihu, aliyense anatenga chofukizira lubani chake nayikamo makala a moto ndi kuthiramo lubani. Iwo anapereka pamaso pa Yehova moto wachilendo, moto umene Yehova sanawalamule. Onani mutuwo |