Levitiko 1:8 - Buku Lopatulika8 ndi ana a Aroni, ansembewo, akonze ziwalozo, mutu, ndi mafuta pa nkhuni zili pa moto wa paguwa la nsembe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 ndi ana a Aroni, ansembewo, akonze ziwalozo, mutu, ndi mafuta pa nkhuni zili pa moto wa pa guwa la nsembe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pamenepo ansembe aike nthuli za nyamayo, mutu wake pamodzi ndi mafuta omwe, pa nkhuni zimene zili pa guwalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kenaka ana a Aaroni, wansembe uja, ayike nthuli za nyamayo, mutu wake pamodzi ndi mafuta omwe pa nkhuni zimene zili paguwapo. Onani mutuwo |