Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 1:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo ana a Aroni wansembeyo asonkhe moto paguwa la nsembe, ndi kukonza nkhuni pamotopo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo ana a Aroni wansembeyo asonkhe moto pa guwa la nsembe, ndi kukonza nkhuni pamotopo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Tsono ansembe, ana a Aroni aja, asonkhe moto pa guwa, ndipo ayalike nkhuni pamotopo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Ndipo ana a Aaroni, wansembe uja asonkhe moto pa guwa ndi kuyalapo nkhuni pa motopo.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 1:7
11 Mawu Ofanana  

Ndipo anafika kumalo komwe Mulungu anamuuza iye; ndipo Abrahamu anamanga guwa la nsembe nakonza nkhuni, namanga Isaki mwana wake, namuika iye paguwa la nsembe pamwamba pa nkhuni.


Ndipo anakonza nkhunizo, naduladula ng'ombe, naiika pankhuni. Nati, Dzazani madzi mbiya zinai, muwathire pa nsembe yopsereza ndi pankhuni.


Ndipo Davide anamangira Yehova guwa la nsembe komweko; napereka nsembe zopsereza, ndi nsembe zoyamika, naitana kwa Yehova; ndipo anamyankha ali m'mwamba ndi moto paguwa la nsembe yopsereza.


mwana wa Elikana, mwana wa Yerohamu, mwana wa Eliyele, mwana wa Towa,


Atatha tsono Solomoni kupemphera, moto unatsika kumwamba, nunyeketsa nsembe yopsereza, ndi nsembe zophera; ndipo ulemerero wa Yehova unadzaza nyumbayi.


ndi chopereka cha nkhuni pa nthawi zoikika, ndi wa zipatso zoyamba. Mundikumbukire, Mulungu wanga, chindikomere.


Ndipo Yehova analankhula ndi Mose, nati,


Ndipo unatuluka moto pamaso ya Yehova, nunyeketsa nsembe yopsereza ndi mafuta paguwa la nsembe; ndipo pakuchiona anthu onse anafuula, nagwa nkhope zao pansi.


Mwenzi atakhala wina mwa inu wakutseka pamakomo, kuti musasonkhe moto chabe paguwa langa la nsembe! Sindikondwera nanu, ati Yehova wa makamu, ndipo sindidzalandira chopereka m'dzanja lanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa