Levitiko 1:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo ana a Aroni wansembeyo asonkhe moto paguwa la nsembe, ndi kukonza nkhuni pamotopo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo ana a Aroni wansembeyo asonkhe moto pa guwa la nsembe, ndi kukonza nkhuni pamotopo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono ansembe, ana a Aroni aja, asonkhe moto pa guwa, ndipo ayalike nkhuni pamotopo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo ana a Aaroni, wansembe uja asonkhe moto pa guwa ndi kuyalapo nkhuni pa motopo. Onani mutuwo |