Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 1:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo asende nsembe yopsereza, ndi kuikadzula ziwalo zake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo asende nsembe yopsereza, ndi kuikadzula ziwalo zake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Ndipo asende nyamayo ndi kuidula nthulinthuli.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Munthuyo asende nsembe yopserezayo ndi kuyidula nthulinthuli.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 1:6
6 Mawu Ofanana  

Yehova Mulungu ndipo anapangira Adamu ndi mkazi wake malaya azikopa, nawaveka iwo.


Ndipo anakonza nkhunizo, naduladula ng'ombe, naiika pankhuni. Nati, Dzazani madzi mbiya zinai, muwathire pa nsembe yopsereza ndi pankhuni.


Ndi zichiri zangowe, chikhato m'litali mwake, zinamangika m'katimo pozungulirapo; ndi pamagome panali nyama ya nsembe.


Ndipo ana a Aroni wansembeyo asonkhe moto paguwa la nsembe, ndi kukonza nkhuni pamotopo;


Uphwanye, nuthirepo mafuta; ndiyo nsembe yaufa.


Ndipo chikopa cha nsembe yopsereza chikhale chakechake cha wansembe, amene anabwera nayo nsembe yopsereza ya munthu aliyense.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa