Levitiko 1:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepo aiphe ng'ombeyo pamaso pa Yehova; ndipo ana a Aroni, ansembewo, abwere nao mwazi, nawaze mwaziwo pozungulira paguwa la nsembe, lokhala pa khoma la chihema chokomanako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo aiphe ng'ombeyo pamaso pa Yehova; ndipo ana a Aroni, ansembewo, abwere nao mwazi, nawaze mwaziwo pozungulira pa guwa la nsembe, lokhala pa khoma la chihema chokomanako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pambuyo pake aiphe pamaso pa Chauta, ndipo ansembe, ana a Aroni, abwere ndi magazi ake. Awaze magaziwo mozungulira guwa limene lili pa khomo la chihema chamsonkhano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pambuyo pake aphe ngʼombeyo pamaso pa Yehova, ndipo ansembe, ana a Aaroni, atenge magazi ake ndi kuwawaza mbali zonse za guwa lansembe limene lili pa khomo la tenti ya msonkhano. Onani mutuwo |