Levitiko 1:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo aiphere iyo pa mbali ya kumpoto ya guwa la nsembe, pamaso pa Yehova; ndipo ana a Aroni, ansembewo, awaze mwazi wake paguwa la nsembe pozungulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo aiphere iyo pa mbali ya kumpoto ya guwa la nsembe, pamaso pa Yehova; ndipo ana a Aroni, ansembewo, awaze mwazi wake pa guwa la nsembe pozungulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndipo aiphere cha kumpoto kwa guwa, pamaso pa Chauta. Tsono ansembe, ana a Aroni, awaze magazi ake pa guwalo molizungulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ayiphere kumpoto kwa guwa, pamaso pa Yehova, ndipo ana a Aaroni amene ndi ansembe, awaze magazi ake mbali zonse za guwalo. Onani mutuwo |