Levitiko 1:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo chopereka chake chikakhala cha nkhosa, kapena cha mbuzi, chikhale nsembe yopsereza; azibwera nayo yaimuna yopanda chilema. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo chopereka chake chikakhala cha nkhosa, kapena cha mbuzi, chikhale nsembe yopsereza; azibwera nayo yaimuna yopanda chilema. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Ngati munthu apereka nsembe yopsereza ya nkhosa kapena mbuzi, ikhale yaimuna yopanda chilema. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “ ‘Koma ngati chopereka cha nsembe yopserezayo ndi nkhosa kapena mbuzi kuchokera pa ziweto zake, munthuyo apereke yayimuna yopanda chilema. Onani mutuwo |