Hoseya 9:8 - Buku Lopatulika8 Efuremu ndiye wozonda kwa Mulungu wanga; kunena za mneneri, msampha wa msodzi uli m'njira zake zonse, ndi udani m'nyumba ya Mulungu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Efuremu ndiye wozonda kwa Mulungu wanga; kunena za mneneri, msampha wa msodzi uli m'njira zake zonse, ndi udani m'nyumba ya Mulungu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mneneri ndiye wochenjeza Aefuremu, anthu a Mulungu wanga. Koma mneneriyo amtchera msampha m'njira zake zonse, ndipo adani akumlalira m'Nyumba ya Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mneneri pamodzi ndi Mulungu wanga ndiwo alonda a Efereimu, koma mneneri amutchera misampha mʼnjira zake zonse, ndipo udani ukumudikira mʼnyumba ya Mulungu wake. Onani mutuwo |