Hoseya 9:5 - Buku Lopatulika5 Mudzachitanji tsiku la misonkhano yoikika, ndi tsiku la chikondwerero cha Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mudzachitanji tsiku la masonkhano oikika, ndi tsiku la chikondwerero cha Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kodi pa tsiku la chikondwerero, tsiku lolemekeza Chauta, anthuwo adzachitapo chiyani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kodi mudzachita chiyani pa tsiku la maphwando anu oyikika; pa masiku a zikondwerero za Yehova? Onani mutuwo |