Hoseya 9:16 - Buku Lopatulika16 Efuremu wakanthidwa, muzu wao wauma, iwo sadzabala zipatso; inde ngakhale abala, koma ndidzapha zipatso zofunika za mimba yao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Efuremu wakanthidwa, muzu wao wauma, iwo sadzabala zipatso; inde ngakhale abala, koma ndidzapha zipatso zofunika za mimba yao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Efuremu ali ngati mtengo wodulidwa umene mizu yake yauma, ndipo sudzabalanso zipatso. Ngakhale anthuwo abale ana, ndidzaŵapha ana ao okondedwawo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Efereimu wathedwa, mizu yake yauma sakubalanso zipatso. Ngakhale atabereka ana, Ine ndidzapha ana awo okondedwawo.” Onani mutuwo |