Hoseya 9:17 - Buku Lopatulika17 Mulungu wanga adzawataya, pakuti sanammvere Iye; ndipo adzakhala othawathawa mwa amitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Mulungu wanga adzawataya, pakuti sanammvere Iye; ndipo adzakhala othawathawa mwa amitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Mulungu wanga adzaŵataya anthu amenewo chifukwa choti sadamumvere. Adzasanduka oyendayenda pakati pa mitundu ya pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mulungu wanga adzawakana chifukwa sanamumvere Iye; adzakhala oyendayenda pakati pa anthu a mitundu ina. Onani mutuwo |