Hoseya 9:12 - Buku Lopatulika12 Angakhale alera ana ao, koma ndidzawasowetsa, wosatsala munthu; ndithunso tsoka iwowa, pamene ndiwachokera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Angakhale alera ana ao, koma ndidzawasowetsa, wosatsala munthu; ndithunso tsoka iwowa, pamene ndiwachokera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ngakhale abale ana, ndidzaŵaononga, sadzakhalapo ndi mmodzi yemwe. Tsoka kwa anthuwo ndikadzaŵasiya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ngakhale atalera ana ndidzachititsa kuti mwana aliyense amwalire. Tsoka kwa anthuwo pamene Ine ndidzawafulatira! Onani mutuwo |