Hoseya 9:11 - Buku Lopatulika11 Kunena za Efuremu, ulemerero wao udzauluka ndi kuchoka ngati mbalame; sipadzakhala kubala, ndi kukhala ndi pakati, ndi kuima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Kunena za Efuremu, ulemerero wao udzauluka ndi kuchoka ngati mbalame; sipadzakhala kubala, ndi kukhala ndi pakati, ndi kuima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ulemerero wa Aefuremu udzaŵathaŵa mouluka ngati mbalame. Sadzabalanso ana. Akazi ao sadzaima, sadzatenga pathupi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ulemerero wa Efereimu udzawuluka ngati mbalame. Sipadzakhalanso kubereka ana, kuyembekezera kapena kutenga pathupi. Onani mutuwo |