Hoseya 9:13 - Buku Lopatulika13 Efuremu, monga ndaona, akunga Tiro, wookedwa pokoma; koma Efuremu adzatulutsira ana ake wakuwaphera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Efuremu, monga ndaona, akunga Tiro, wookedwa pokoma; koma Efuremu adzatulutsira ana ake wakuwaphera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Inu Chauta, monga ndikuwonera, ana a Efuremu adzakhala ngati nyama zojiwa. Aefuremu adzatsogolera ana ao kunkhondo kumene adzaphedwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndaona Efereimu ngati Turo, atadzalidwa pa nthaka ya chonde. Koma Efereimu adzatsogolera ana ake kuti akaphedwe.” Onani mutuwo |