Hoseya 8:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti anakwera kunka ku Asiriya, ngati mbidzi ya pa yokha mwini wake; Efuremu walembera omkonda ngati antchito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti anakwera kunka ku Asiriya, ngati mbidzi ya pa yokha mwini wake; Efuremu walembera omkonda ngati antchito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Adathaŵira ku Asiriya ngati mbidzi yongodziyendera payokha. Aefuremu adalipira anthu a ku maiko ena kuti akhale oŵathandiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pakuti iwo anapita ku Asiriya ngati mbidzi yongodziyendera pa yokha. Efereimu wadzigulitsa kwa zibwenzi zake. Onani mutuwo |