Hoseya 8:10 - Buku Lopatulika10 Inde angakhale alembera mwa amitundu ndidzawasonkhanitsa tsopano; ndipo ayamba kuchepa chifukwa cha katundu wa mfumu ya akalonga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Inde angakhale alembera mwa amitundu ndidzawasonkhanitsa tsopano; ndipo ayamba kuchepa chifukwa cha katundu wa mfumu ya akalonga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chifukwa choti adagwirizana ndi anthu a mitundu ina, ndidzaŵasonkhanitsa ndi kuŵaononga. Posachedwa adzazunzika kwambiri chifukwa cha ulamuliro wa mfumu ya ku Asiriya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ngakhale wadzigulitsa pakati pa mitundu ya anthu, Ine ndidzawasonkhanitsa pamodzi. Iwo adzayamba kuzunzika pansi pa ulamuliro wankhanza wa mfumu yamphamvu. Onani mutuwo |