Hoseya 8:11 - Buku Lopatulika11 Popeza Efuremu anachulukitsa maguwa a nsembe akuchimwako, maguwa a nsembe omwewo anamchimwitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Popeza Efuremu anachulukitsa maguwa a nsembe akuchimwako, maguwa a nsembe omwewo anamchimwitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Aefuremu adachulukitsa maguwa ansembe ochotserapo machimo, koma maguwawo asanduka malo ochimwirapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Ngakhale Efereimu anamanga maguwa ambiri a nsembe zoperekedwa chifukwa cha tchimo, maguwa amenewa akhala malo ochimwirapo. Onani mutuwo |