Hoseya 8:12 - Buku Lopatulika12 Ndinamlembera zinthu zambirimbirizo za chilamulo changa, koma zinayesedwa ngati chinthu chachilendo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndinamlembera zinthu zambirimbirizo za chilamulo changa, koma zinayesedwa ngati chinthu chachilendo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndidaŵapatsa malamulo ambiri olembedwa, koma saŵasamala. Amaŵayesa achilendo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndinawalembera zinthu zambiri za malamulo anga, koma iwo anaziyesa ngati zinthu zachilendo. Onani mutuwo |