Hoseya 8:13 - Buku Lopatulika13 Kunena za nsembe za zopereka zanga, aphera nsembe yanyama, naidya; koma Yehova sazilandira; tsopano adzakumbukira mphulupulu yao, nadzalanga zochimwa zao; adzabwerera kunka ku Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Kunena za nsembe za zopereka zanga, aphera nsembe yanyama, naidya; koma Yehova sazilandira; tsopano adzakumbukira mphulupulu yao, nadzalanga zochimwa zao; adzabwerera kunka ku Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Amapereka nsembe zanyama kwa Ine nkumadya, koma Ine Chauta sindikondwera nazo konse. Sindidzaiŵala zolakwa zao, ndidzaŵalanga chifukwa cha zimenezo. Ndidzaŵabwezera ku ukapolo ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Amapereka nsembe za nyama kwa Ine ndipo iwo amadya nyamayo, koma Yehova sakondwera nazo. Tsopano Iye adzakumbukira zoyipa zawo ndi kuwalanga chifukwa cha machimo awo: iwowo adzabwerera ku Igupto. Onani mutuwo |