Hoseya 8:8 - Buku Lopatulika8 Israele wamezedwa; tsopano ali mwa amitundu ngati chotengera choti munthu sakondwera nacho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Israele wamezedwa; tsopano ali mwa amitundu ngati chotengera choti munthu sakondwera nacho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Aisraele amezedwa. Asanduka ngati chiŵiya chachabe pakati pa anthu a mitundu ina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Israeli wamezedwa, tsopano ali pakati pa anthu a mitundu ina ngati chinthu cha chabechabe. Onani mutuwo |