Hoseya 8:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti abzala mphepo, nadzakolola kamvulumvulu; alibe tirigu wosasenga; ngala siidzatulutsa ufa; chinkana iutulutsa, alendo adzaumeza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti abzala mphepo, nadzakolola kamvulumvulu; alibe tirigu wosasenga; ngala siidzatulutsa ufa; chinkana iutulutsa, alendo adzaumeza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Aisraele amafesa kamphepo, ndipo amakolola kamvulumvulu. Tirigu alibe ngala, sadzabala chakudya. Akadabala, alendo akadadya chakudyacho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Aisraeli amadzala mphepo ndipo amakolola kamvuluvulu. Tirigu alibe ngala; sadzabala chakudya. Akanabala chakudya alendo akanadya chakudyacho. Onani mutuwo |