Hoseya 8:5 - Buku Lopatulika5 Mwanawang'ombe wako wakutaya, Samariya iwe; mkwiyo wanga wayakira iwo; adzalephera kuyera mtima mpaka liti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mwanawang'ombe wako wakutaya, Samariya iwe; mkwiyo wanga wayakira iwo; adzalephera kuyera mtima mpaka liti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Fano la mwanawang'ombe limene a ku Samariya akupembedza likundinyansa. Motero mkwiyo wanga waŵayakira kwambiri anthuwo. Padzapita nthaŵi yaitali chotani asanasinthe kuti ayere anthu a ku Israele? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iwe Samariya, taya fano lako la mwana wangʼombe! Mkwiyo wanga wayakira anthuwo. Padzapita nthawi yayitali chotani asanasinthike kukhala oyera mtima? Onani mutuwo |