Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Hoseya 8:3 - Buku Lopatulika

3 Israele wachitaya chokoma, mdani adzamlondola.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Israele wachitaya chokoma, mdani adzamlondola.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Koma Aisraele akana zabwino. Nchifukwa chake adani ao adzaŵapirikitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Koma Israeli wakana zabwino; mdani adzamuthamangitsa.

Onani mutuwo Koperani




Hoseya 8:3
10 Mawu Ofanana  

Mau a pakamwa pake ndiwo opanda pake ndi onyenga, waleka kuzindikira ndi kuchita bwino.


mudzawalondola mokwiya ndi kuwaononga pansi pa thambo la Yehova.


Otilondola anaposa ziombankhanga za m'mlengalenga m'liwiro lao, anatithamangitsa pamapiri natilalira m'chipululu.


Adzafuulira kwa Ine, Mulungu wanga, ife Aisraele tikudziwani.


Analonga mafumu, koma sikunachokera kwa Ine; anaika akalonga, koma sindinadziwa; anadzipangira mafano a siliva wao ndi golide wao, kuti akalikhidwe.


Kunena za iwo akutsalira, ndidzalonga kukomoka kumtima kwao m'maiko a adani ao; ndi liu la tsamba lotengeka ndi mphepo lidzawapirikitsa; ndipo adzathawa monga amathawa lupanga; ndipo adzagwa wopanda wakuwalondola.


Atero Yehova, Chifukwa cha zolakwa zitatu za Edomu, kapena zinani, sindidzabweza kulanga kwake; popeza analondola mphwake ndi lupanga, nafetsa chifundo chake chonse, ndi mkwiyo wake unang'amba ching'ambire nasunga mkwiyo wake chisungire;


Yehova adzalola adani anu akukantheni; mudzawatulukira njira imodzi, koma mudzawathawa pamaso pao njira zisanu ndi ziwiri, ndipo mudzagwedezeka pakati pa maufumu onse a dziko lapansi.


pokhala nacho chitsutso, popeza adataya chikhulupiriro chao choyamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa