Hoseya 8:2 - Buku Lopatulika2 Adzafuulira kwa Ine, Mulungu wanga, ife Aisraele tikudziwani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Adzafuulira kwa Ine, Mulungu wanga, ife Aisraele tikudziwani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Amalirira kwa Ine kuti ndiŵathandize, amati, ‘Ife Aisraele tikukudziŵani Inu Mulungu wathu.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Israeli akulirira kwa Ine kuti, ‘Inu Mulungu wathu, ife timakudziwani!’ Onani mutuwo |