Hoseya 8:1 - Buku Lopatulika1 Lipenga kukamwa kwako. Akudza ngati chiombankhanga, kulimbana ndi nyumba ya Yehova; chifukwa analakwira chipangano changa, napikisana nacho chilamulo changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Lipenga kukamwa kwako. Akudza ngati chiombankhanga, kulimbana ndi nyumba ya Yehova; chifukwa analakwira chipangano changa, napikisana nacho chilamulo changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta akuti, “Lizani lipenga! Adani akugudukira dziko la Chauta ngati adembo pamwamba pa nyama. Anthu anga aphwanya chipangano changa, ndipo achimwira malamulo anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Ika lipenga pakamwa pako. Ngati chiwombankhanga, kutsutsana ndi nyumba ya Yehova chifukwa anthu aphwanya pangano langa ndiponso agalukira lamulo langa. Onani mutuwo |